Pomwe nkhani ya katangale pakati pa oweruza milandu komaso oyimilira anthu pa milandu ikupitilira, nduna ya zachilungamo Titus Mvalo, wayikira kumbuyo oweruza milandu awiri omwe akuganizilidwa kuti amapanga katangale. Poyikira mlomo pa gulu lina la pa WhatsApp za mndandanda wa oweruza milandu omwe akuganizilidwa kuti akhala akupanga katangale, Mvalo wati oweruza milandu Nyakaunda Kamanga ndi […]
The post Ma Jaji awiriwa achotseni si a chinyengo - Mvalo appeared first on Malawi 24.